Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 103:3 - Buku Lopatulika

3 Amene akhululukira mphulupulu zako zonse; nachiritsa nthenda zako zonse;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

3 Amene akhululukira mphulupulu zako zonse; nachiritsa nthenda zako zonse;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

3 Ndiye amene amakhululukira machimo ako onse, ndi kuchiritsa matenda ako onse.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

3 Amene amakhululuka machimo ako onse ndi kuchiritsa nthenda zako zonse,

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 103:3
27 Mawu Ofanana  

Ndipo Davide anati kwa Natani, Ndinachimwira Yehova. Natani nati kwa Davide, Ndiponso Yehova wachotsa tchimo lanu, simudzafa.


Koma kwa Inu kuli chikhululukiro, kuti akuopeni.


Ndipo adzaombola Israele ku mphulupulu zake zonse.


Achiritsa osweka mtima, namanga mabala ao.


Yehova, Mulungu wanga, ndinafuulira kwa Inu, ndipo munandichiritsa.


Chamgwera chinthu choopsa, ati; popeza ali gonire sadzaukanso.


Pakuti Inu, Ambuye, ndinu wabwino, ndi wokhululukira, ndi wa chifundo chochulukira onse akuitana Inu.


ndipo anati, Ngati udzamveratu mau a Yehova, Mulungu wako, ndi kuchita zoona pamaso pake, ndi kutchera khutu pa malamulo ake, ndi kusunga malemba ake onse, za nthenda zonse ndinaziika pa Aejipito sindidzaziika pa iwe nnena imodzi; pakuti Ine Yehova ndine wakuchiritsa iwe.


wakusungira anthu osawerengeka chifundo, wakukhululukira mphulupulu ndi kulakwa ndi kuchimwa; koma wosamasula wopalamula; wakulanga ana ndi zidzukulu chifukwa cha mphulupulu ya atate ao, kufikira mbadwo wachitatu ndi wachinai.


Ndipo wokhalamo sadzanena, Ine ndidwala; anthu okhala m'menemo, adzakhululukidwa mphulupulu zao.


Taonani, ndinali ndi zowawa zazikulu, chifukwa cha mtendere wanga; Koma Inu mokonda moyo wanga, munaupulumutsa m'dzanja la chivundi, Pakuti mwaponya m'mbuyo mwanu machimo anga onse.


Ine, Inedi, ndine amene ndifafaniza zolakwa zako, chifukwa cha Ine mwini; ndipo Ine sindidzakumbukira machimo ako.


Koma Iye analasidwa chifukwa cha zolakwa zathu, natundudzidwa chifukwa cha mphulupulu zathu; chilango chotitengera ife mtendere chinamgwera Iye; ndipo ndi mikwingwirima yake ife tachiritsidwa.


Mundichiritse ine, Yehova, ndipo ndidzachiritsidwa; mundipulumutse ine, ndipo ndidzapulumutsidwa; pakuti chilemekezo changa ndinu.


Ndipo Mose anafuulira kwa Yehova, ndi kuti, Mchiritsenitu, Mulungu.


Ndipo Yesu pakuona chikhulupiriro chao ananena ndi wodwala manjenje, Mwana, machimo ako akhululukidwa.


Tili ndi maomboledwe mwa mwazi wake, chikhululukiro cha zochimwa, monga mwa kulemera kwa chisomo chake,


ndipo pemphero la chikhulupiriro lidzapulumutsa wodwalayo, ndipo Ambuye adzamuukitsa; ndipo ngati adachita machimo adzakhululukidwa kwa iye.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa