Masalimo 147:3 - Buku Lopatulika3 Achiritsa osweka mtima, namanga mabala ao. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Achiritsa osweka mtima, namanga mabala ao. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Akuchiritsa a mtima wachisoni, ndipo akumanga mabala ao. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Akutsogolera anthu osweka mtima ndi kumanga mabala awo. Onani mutuwo |