Masalimo 147:4 - Buku Lopatulika4 Awerenga nyenyezi momwe zili; azitcha maina zonsezi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Awerenga nyenyezi momwe zili; azitcha maina zonsezi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Amadziŵa chiŵerengero cha nyenyezi, zonse amazitcha maina ake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Amadziwa chiwerengero cha nyenyezi, ndipo iliyonse amayitchula dzina. Onani mutuwo |