Masalimo 147:5 - Buku Lopatulika5 Ambuye wathu ndi wamkulu ndi wa mphamvu zambiri; nzeru yake njosatha. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Ambuye wathu ndi wamkulu ndi wa mphamvu zambiri; nzeru yake njosatha. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Mbuye wathu ndi wamkulu, ndipo ndi wa mphamvu zambiri, nzeru zake nzopanda malire. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Yehova ndi wamkulu ndi wamphamvu kwambiri; nzeru zake zilibe malire. Onani mutuwo |