Hoseya 6:1 - Buku Lopatulika1 Tiyeni, tibwerere kunka kwa Yehova; pakuti wang'amba, nadzatipoletsera; wakantha, nadzatimanga. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Tiyeni, tibwerere kunka kwa Yehova; pakuti wang'amba, nadzatipoletsera; wakantha, nadzatimanga. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Anthu akunena kuti, “Tiyeni, tibwerere kwa Chauta. Watikadzula, komabe adzatichiritsa. Watikantha, komabe adzamanga mabala athu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 “Bwerani, tiyeni tibwerere kwa Yehova. Iye watikhadzula, koma adzatichiritsa. Iye wativulaza, koma adzamanga mabala athu. Onani mutuwo |