Hoseya 5:15 - Buku Lopatulika15 Ndidzamuka ndi kubwerera kunka kumalo kwanga, mpaka adzavomereza kupalamula kwao, nafunafuna nkhope yanga; m'msauko mwao adzandifunafuna mwachangu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201415 Ndidzamuka ndi kubwerera kunka kumalo kwanga, mpaka adzavomereza kupalamula kwao, nafunafuna nkhope yanga; m'msauko mwao adzandifunafuna mwachangu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa15 “Ndidzabwerera ku malo anga, mpaka anthu anga atasaukiratu, ndi kuyamba kundifunafuna. M'mavuto ao adzayesetsa kundipeza.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero15 Ndipo ndidzabwerera ku malo anga mpaka anthu anga atavomereza kulakwa kwawo. Ndipo iwo adzafunafuna nkhope yanga; mʼmasautso awo adzandifunitsitsa Ine.” Onani mutuwo |