Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 3:1 - Buku Lopatulika

Yehova! Ha! Achuluka nanga akundisautsa ine! Akundiukira ine ndi ambiri.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Yehova! Ha! Achuluka nanga akundisautsa ine! Akundiukira ine ndi ambiri.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Inu Chauta, ndili ndi adani ochuluka, anthu ambiri akundiwukira.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Inu Yehova, achulukadi adani anga! Achulukadi amene andiwukira!

Onani mutuwo



Masalimo 3:1
7 Mawu Ofanana  

Ndipo Abisalomu, ndi anthu onse aamuna a Israele, anafika ku Yerusalemu, ndi Ahitofele pamodzi naye.


Onetsani chifundo chanu chodabwitsa, Inu wakupulumutsa okhulupirira Inu kwa iwo akuwaukira ndi dzanja lanu lamanja.


Ndipo mbale adzapereka mbale wake kuimfa, ndi atate mwana wake: ndipo ana adzatsutsa akuwabala, nadzawafetsa iwo.


Ndipo anthu onse anavomereza, ndi kuti, Mwazi wake uli pa ife ndi pa ana athu.


Ndipo mafumu awa onse anasonkhana, nadza namanga pamodzi ku madzi a Meromu, kumthira Israele nkhondo.