Mateyu 10:21 - Buku Lopatulika21 Ndipo mbale adzapereka mbale wake kuimfa, ndi atate mwana wake: ndipo ana adzatsutsa akuwabala, nadzawafetsa iwo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201421 Ndipo mbale adzapereka mbale wake kuimfa, ndi atate mwana wake: ndipo ana adzatsutsa akuwabala, nadzawafetsa iwo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa21 “Mbale azidzapereka mbale wake kuti aphedwe, bambo azidzapereka mwana wake. Ana adzaukira makolo ao, mpaka kuŵaphetsa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero21 “Mʼbale adzapereka mʼbale kuti aphedwe ndi abambo mwana wawo: ndipo ana adzawukira makolo awo ndi kuwapereka kuti aphedwe. Onani mutuwo |