Mateyu 10:22 - Buku Lopatulika22 Ndipo adzada inu anthu onse chifukwa cha dzina langa; koma iye wakupirira kufikira chimaliziro, iyeyu adzapulumutsidwa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201422 Ndipo adzada inu anthu onse chifukwa cha dzina langa; koma iye wakupirira kufikira chimaliziro, iyeyu adzapulumutsidwa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa22 Anthu onse adzadana nanu chifukwa cha Ine. Koma yemwe adzalimbikire mpaka potsiriza, ameneyo ndiye adzapulumuke. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero22 Anthu onse adzada inu chifukwa cha Ine, koma iye amene apirira mpaka kumapeto, adzapulumuka. Onani mutuwo |