Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 3:2 - Buku Lopatulika

2 Ambiri amati kwa moyo wanga, alibe chipulumutso mwa Mulungu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

2 Ambiri amati kwa moyo wanga, alibe chipulumutso mwa Mulungu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

2 Anthu ambiri akamalankhula za ine amati, “Mulungu samupulumutsa.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

2 Ambiri akunena za ine kuti, “Mulungu sadzamupulumutsa.” Sela

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 3:2
14 Mawu Ofanana  

Akadapanda kukhala nafe Yehova, pakutiukira anthu:


Onse akundipenya andiseka; akwenzula, apukusa mutu, nati,


Ndifuula kwa Yehova ndi mau anga, ndipo andiyankha m'phiri lake loyera.


Chipulumutso ncha Yehova; dalitso lanu likhale pa anthu anu.


Amuna inu, ulemu wanga udzakhala wamanyazi kufikira liti? Mudzakonda zachabe, ndi kufunafuna bodza kufikira liti?


Chitani chinthenthe, ndipo musachimwe. Nenani mumtima mwanu pakama panu, ndipo mukhale chete.


Adani anga andinyoza ndi kundithyola mafupa anga; pakunena ndine dzuwa lonse, Mulungu wako ali kuti?


Misozi yanga yakhala ngati chakudya changa, usana ndi usiku; pakunena iwo kwa ine dzuwa lonse, Mulungu wako ali kuti?


ndi kuti, Wamsiya Mulungu. Mlondoleni, mgwireni; popeza palibe wompulumutsa.


Munatulukira chipulumutso cha anthu anu, chipulumutso cha odzozedwa anu; munakantha mutu wa nyumba ya woipa, ndi kufukula maziko kufikira m'khosi.


Mulungu anafuma ku Temani, ndi Woyerayo kuphiri la Parani. Ulemerero wake unaphimba miyamba, ndi dziko lapansi linadzala ndi kumlemekeza.


Munapombosola uta wanu; malumbiro analumbirira mafuko anali mau oona. Munang'amba dziko lapansi ndi mitsinje.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa