Masalimo 3:2 - Buku Lopatulika2 Ambiri amati kwa moyo wanga, alibe chipulumutso mwa Mulungu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Ambiri amati kwa moyo wanga, alibe chipulumutso mwa Mulungu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Anthu ambiri akamalankhula za ine amati, “Mulungu samupulumutsa.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Ambiri akunena za ine kuti, “Mulungu sadzamupulumutsa.” Sela Onani mutuwo |