Masalimo 3:1 - Buku Lopatulika1 Yehova! Ha! Achuluka nanga akundisautsa ine! Akundiukira ine ndi ambiri. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Yehova! Ha! Achuluka nanga akundisautsa ine! Akundiukira ine ndi ambiri. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Inu Chauta, ndili ndi adani ochuluka, anthu ambiri akundiwukira. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Inu Yehova, achulukadi adani anga! Achulukadi amene andiwukira! Onani mutuwo |