Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yoswa 11:5 - Buku Lopatulika

5 Ndipo mafumu awa onse anasonkhana, nadza namanga pamodzi ku madzi a Meromu, kumthira Israele nkhondo.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

5 Ndipo mafumu awa onse anasonkhana, nadza namanga pamodzi ku madzi a Meromu, kumthira Israele nkhondo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

5 Mafumu onseŵa adasonkhana pamodzi, nakamanga zithando ku mtsinje wa Meromu, kuti alimbane ndi Aisraele.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

5 Mafumu onsewa anasonkhana pamodzi ndipo anamanga misasa yawo ku mtsinje wa Meromu, kuti amenyane ndi Israeli.

Onani mutuwo Koperani




Yoswa 11:5
9 Mawu Ofanana  

Ndipo pamene Aaramu anaona kuti Aisraele anawathyola, anasonkhana pamodzi.


Yehova! Ha! Achuluka nanga akundisautsa ine! Akundiukira ine ndi ambiri.


Anapenya mudziwo, ndipo pamenepo anadabwa; anaopsedwa, nathawako.


Chitani phokoso, anthu inu, koma mudzathyokathyoka; tcherani khutu, inu nonse a maiko akutali; kwindani nokha, koma mudzathyokathyoka; kwindani nokha, koma mudzathyokathyoka.


Ndipo anatuluka, iwo ndi makamu ao onse nao, anthu ambiri, kuchuluka kwao ngati mchenga uli m'mphepete mwa nyanja; ndi akavalo ndi magaleta ambirimbiri.


Koma Yehova anati kwa Yoswa, Usaope chifukwa cha iwowa; pakuti mawa, dzuwa lino ndidzawapereka onse ophedwa pamaso pa Israele; udzawadula mitsindo akavalo ao, ndi kutentha agaleta ao ndi moto.


anasonkhana kuponyana ndi Yoswa ndi Israele, ndi mtima umodzi.


pakuti ali mizimu ya ziwanda zakuchita zizindikiro; zimene zituluka kunka kwa mafumu a dziko lonse, kuwasonkhanitsira kunkhondo ya tsiku lalikulu la Mulungu, Wamphamvuyonse.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa