Mateyu 27:25 - Buku Lopatulika25 Ndipo anthu onse anavomereza, ndi kuti, Mwazi wake uli pa ife ndi pa ana athu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201425 Ndipo anthu onse anavomereza, ndi kuti, Mwazi wake uli pa ife ndi pa ana athu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa25 Anthu onse aja adati, “Imfayo mlandu wake ugwere ife ndi ana athu.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero25 Anthu onse anayankha nati, “Magazi ake akhale pa ife ndi pa ana athu!” Onani mutuwo |
Ndipo Yehova adzambwezera mwazi wake pamutu wake wa iye yekha, popeza iye anawakantha anthu awiri olungama ndi okoma oposa iye mwini, nawapha ndi lupanga, atate wanga Davide osadziwa, ndiwo Abinere mwana wa Nere kazembe wa khamu la nkhondo la Israele, ndi Amasa mwana wa Yetere kazembe wa khamu la nkhondo la Yuda.