Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 127:4 - Buku Lopatulika

Ana a ubwana wake wa munthu akunga mivi m'dzanja lake la chiphona.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ana a ubwana wake wa munthu akunga mivi m'dzanja lake la chiphona.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Ana apaunyamata ali ngati mivi m'manja mwa munthu wankhondo.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ana a pa unyamata ali ngati mivi mʼmanja mwa munthu wankhondo.

Onani mutuwo



Masalimo 127:4
4 Mawu Ofanana  

Mivi yakuthwa ya chiphona, ndi makala tsanya.


Zidzukulu ndizo korona wa okalamba; ndipo ulemerero wa ana ndiwo atate ao.


Anake adzanyamuka, nadzamutcha wodala; mwamuna wake namtama, nati,


Pakuti, taonani, ndidzabukitsa ndidzafikitsa kudzamenyana ndi Babiloni msonkhano wa mitundu yaikulu kuchokera kudziko la kumpoto; ndipo adzaguba pomenyana ndi iye; kumeneko Babiloni adzachotsedwa; mivi yao idzakhala ngati ya munthu wamaluli wamphamvu; yosabwera chabe.