Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 127:4 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

4 Ana a pa unyamata ali ngati mivi mʼmanja mwa munthu wankhondo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

4 Ana a ubwana wake wa munthu akunga mivi m'dzanja lake la chiphona.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

4 Ana a ubwana wake wa munthu akunga mivi m'dzanja lake la chiphona.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

4 Ana apaunyamata ali ngati mivi m'manja mwa munthu wankhondo.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 127:4
4 Mawu Ofanana  

Adzakulangani ndi mivi yakuthwa ya munthu wankhondo, ndi makala oyaka a mtengo wa tsanya.


Zidzukulu ndiye ulemu wa anthu okalamba, ndipo makolo ndiye ulemerero wa ana.


Ana ake amamunyadira ndipo amamutcha kuti wodala; ndipo mwamuna wake, amamuyamikira nʼkumati,


Taonani, ndidzaukitsa gulu lankhondo lamphamvu la mitundu ina ndi kubwera nalo kuchokera kumpoto kudzamenyana ndi Babuloni. Iwo adzandandalika ankhondo awo ndi kugonjetsa Babuloni. Mivi yawo ili ngati ya ankhondo aluso, yosapita padera.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa