Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Masalimo 127:5 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

5 Wodala munthu amene motengera mivi mwake mwadzaza. Iwo sadzachititsidwa manyazi pamene alimbana ndi adani awo pa zipata.

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

5 Wodala munthu amene anadzaza nayo phodo lake: sadzachita manyazi iwo, pakulankhula nao adani kuchipata.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

5 Wodala munthu amene anadzaza nayo phodo lake: sadzachita manyazi iwo, pakulankhula nao adani kuchipata.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

5 Ngwodala amene phodo lake nlodzaza ndi mivi yotere. Sadzamchititsa manyazi akamalankhula ndi adani ake pa bwalo lamilandu.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 127:5
6 Mawu Ofanana  

ndipo anaona mʼbado wachitatu wa ana a Efereimu. Yosefe anatenganso ana a Makiri, mwana wa Manase kukhala ngati ana a mʼbanja lake.


Anali ndi ana aamuna asanu ndi awiri ndi ana aakazi atatu,


Ana ake alibe ndi chitetezo chomwe; amaponderezedwa mʼbwalo la milandu popanda owateteza.


Iye ndi Mulungu amene amabwezera chilango, amene amagonjetsa anthu a mitundu yonse amene ali pansi pa ulamuliro wanga,


Mwana wanga, khala wanzeru, ndipo ukondweretse mtima wanga; pamenepo ine ndidzatha kuyankha aliyense amene amandinyoza.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa