Masalimo 120:4 - Buku Lopatulika4 Mivi yakuthwa ya chiphona, ndi makala tsanya. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Mivi yakuthwa ya chiphona, ndi makala tsanya. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Adzakuzunzani ndi mivi yakuthwa ya munthu wankhondo, pamodzi ndi makala amoto a mtengo wa tsanya. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Adzakulangani ndi mivi yakuthwa ya munthu wankhondo, ndi makala oyaka a mtengo wa tsanya. Onani mutuwo |