Masalimo 120:5 - Buku Lopatulika5 Tsoka ine, kuti ndili mlendo mu Meseki, kuti ndigonera m'mahema a Kedara! Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Tsoka ine, kuti ndili mlendo m'Meseki, kuti ndigonera m'mahema a Kedara! Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Ndili ndi tsoka lalikulu, chifukwa ndimakhala pakati pa anthu onga mbuli za ku Meseki ndi Kedara. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Tsoka ine kuti ndimakhala ku Mesaki, kuti ndimakhala pakati pa matenti a ku Kedara! Onani mutuwo |