Masalimo 120:6 - Buku Lopatulika6 Moyo wanga unakhalitsa nthawi pamodzi ndi iye wakudana nao mtendere. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Moyo wanga unakhalitsa nthawi pamodzi ndi iye wakudana nao mtendere. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Ndakhala nthaŵi yaitali pakati pa anthu odana ndi mtendere. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Kwa nthawi yayitali ndakhala pakati pa iwo amene amadana ndi mtendere. Onani mutuwo |