Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 118:8 - Buku Lopatulika

Kuthawira kwa Yehova nkokoma koposa kukhulupirira munthu.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Kuthawira kwa Yehova nkokoma koposa kukhulupirira munthu.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Kuthaŵira kwa Chauta nkwabwino kupambana kukhulupirira munthu.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Nʼkwabwino kuthawira kwa Yehova kusiyana ndi kudalira munthu.

Onani mutuwo



Masalimo 118:8
6 Mawu Ofanana  

Ndipo iye anati, Ndikupatsa iwe bwanji? Ndipo Yakobo anati, Usandipatse ine kanthu; ukandichitira ine chotero, ine ndidzadyetsanso ndi kusunganso ziweto zako.


Musamakhulupirira zinduna, kapena mwana wa munthu, amene mulibe chipulumutso mwa iye.


Wodala munthuyo wakuyesa Yehova wokhulupirika; wosasamala odzikuza, ndi opatukira kubodza.