Masalimo 118:9 - Buku Lopatulika9 Kuthawira kwa Yehova nkokoma koposa kukhulupirira akulu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Kuthawira kwa Yehova nkokoma koposa kukhulupirira akulu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Kuthaŵira kwa Chauta nkwabwino kupambana kukhulupirira mafumu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Nʼkwabwino kuthawira kwa Yehova kusiyana ndi kudalira mafumu. Onani mutuwo |