Masalimo 118:10 - Buku Lopatulika10 Amitundu onse adandizinga, zedi, m'dzina la Yehova ndidzawaduladula. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Amitundu onse adandizinga, zedi, m'dzina la Yehova ndidzawaduladula. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Adani a mitundu yonse adandizinga, koma ndidaŵaononga ndi mphamvu za dzina la Chauta. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Anthu a mitundu yonse anandizinga, koma mʼdzina la Yehova ndinawawononga. Onani mutuwo |