Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 113:2 - Buku Lopatulika

Lodala dzina la Yehova Kuyambira tsopano kufikira kosatha.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Lodala dzina la Yehova Kuyambira tsopano kufikira kosatha.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Yamikani Chauta kuyambira tsopano mpaka muyaya.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Yehova atamandidwe, kuyambira tsopano mpaka muyaya.

Onani mutuwo



Masalimo 113:2
8 Mawu Ofanana  

Alemekezedwe Yehova Mulungu wa Israele, kuyambira kosayamba kufikira kosatha. Ndipo anthu onse anati, Amen! Nalemekeza Yehova.


Wodala Yehova, Mulungu wa Israele, kuyambira kosayamba kufikira kosatha. Ndi anthu onse anene, Amen. Aleluya.


Koma ife tidzalemekeza Yehova kuyambira tsopano kufikira nthawi yonse. Aleluya.


Wodalitsika Yehova, Mulungu wa Israele, kuchokera nthawi yosayamba kufikira nthawi yosatha. Amen, ndi Amen.


Daniele anayankha, nati, Lilemekezedwe dzina la Mulungu kunthawi za nthawi, pakuti nzeru ndi mphamvu zili zake;


kwa Iye ukhale ulemerero mu Mpingo ndi mwa Khristu Yesu, kufikira mibadwo yonse ya nthawi za nthawi. Amen.


Ndipo cholengedwa chilichonse chili m'mwamba, ndi padziko, ndi pansi padziko, ndi m'nyanja, ndi zonse zili momwemo, ndinazimva zilikunena, Kwa Iye wakukhala pa mpando wachifumu, ndi kwa Mwanawankhosa zikhale chiyamiko, ndi ulemu, ndi ulemerero, ndi mphamvu, kufikira nthawi za nthawi.