Masalimo 41:13 - Buku Lopatulika13 Wodalitsika Yehova, Mulungu wa Israele, kuchokera nthawi yosayamba kufikira nthawi yosatha. Amen, ndi Amen. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Wodalitsika Yehova, Mulungu wa Israele, kuchokera nthawi yosayamba kufikira nthawi yosatha. Amen, ndi Amen. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Atamandike Chauta, Mulungu wa Israele, kuyambira muyaya mpaka muyaya. Inde momwemo. Inde momwemo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Atamandike Yehova Mulungu wa Israeli kuchokera muyaya mpaka muyaya. Ameni ndi Ameni. Onani mutuwo |