Masalimo 41:12 - Buku Lopatulika12 Ndipo ine, mundigwirizize mu ungwiro wanga, ndipo mundiike pankhope panu kunthawi yamuyaya. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Ndipo ine, mundigwirizize m'ungwiro wanga, ndipo mundiike pankhope panu kunthawi yamuyaya. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Inu mwandichirikiza chifukwa cha kukhulupirika kwanga, mwandikhazika pamaso panu mpaka muyaya. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Mu ungwiro wanga Inu mumandisunga ndi kundiyimika pamaso panu kwamuyaya. Onani mutuwo |