Masalimo 41:11 - Buku Lopatulika11 Umo ndidziwa kuti mukondwera ndi ine, popeza mdani wanga sandiseka. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Umo ndidziwa kuti mukondwera ndi ine, popeza mdani wanga sandiseka. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Mukatero ndidzadziŵa kuti mumakondwera nane, chifukwa mdani wanga sadandipambane. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Ine ndikudziwa kuti mukukondwera nane, pakuti mdani wanga sandigonjetsa. Onani mutuwo |