Masalimo 115:18 - Buku Lopatulika18 Koma ife tidzalemekeza Yehova kuyambira tsopano kufikira nthawi yonse. Aleluya. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 Koma ife tidzalemekeza Yehova kuyambira tsopano kufikira nthawi yonse. Aleluya. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 Koma ife tidzatamanda Chauta kuyambira tsopano mpaka muyaya. Tamandani Chauta! Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 ndi ife amene timatamanda Yehova, kuyambira tsopano mpaka muyaya. Tamandani Yehova. Onani mutuwo |