Masalimo 113:1 - Buku Lopatulika1 Aleluya; Lemekezani, inu atumiki a Yehova; lemekezani dzina la Yehova. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Aleluya; Lemekezani, inu atumiki a Yehova; lemekezani dzina la Yehova. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Tamandani Chauta! Mtamandeni, inu atumiki ake, tamandani dzina la Chauta. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Tamandani Yehova. Mutamandeni, inu atumiki a Yehova, tamandani dzina la Yehova. Onani mutuwo |