Masalimo 112:10 - Buku Lopatulika10 Woipa adzaziona, nadzapsa mtima; adzakukuta mano, nadzasungunuka; chokhumba oipa chidzatayika. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Woipa adzaziona, nadzapsa mtima; adzakukuta mano, nadzasungunuka; chokhumba oipa chidzatayika. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Munthu woipa amaona zimenezi, ndipo amapsa nazo mtima. Amakukuta mano nazimirira. Zokhumba za munthu woipa sizidzachitika konse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Munthu woyipa adzaona zimenezi ndipo adzapsa mtima; adzakukuta mano ake ndipo adzasungunuka. Zolakalaka za anthu oyipa sizidzachitika konse. Onani mutuwo |