Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 11:3 - Buku Lopatulika

Akapasuka maziko, wolungama angachitenji?

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Akapasuka maziko, wolungama angachitenji?

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Tsono ngati maziko aonongeka, nanga wolungama angachite chiyani?”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Tsono ngati maziko awonongeka, olungama angachite chiyani?”

Onani mutuwo



Masalimo 11:3
15 Mawu Ofanana  

Koma wolungama asungitsa njira yake, ndi iye wa manja oyera adzakulabe mumphamvu.


Lasungunuka dziko lapansi, ndi onse okhalamo; ndinachirika mizati yake.


Sadziwa, ndipo sazindikira; amayendayenda mumdima; maziko onse a dziko lapansi agwedezeka.


Ndipo iwo amene adzakhala a iwe adzamanga malo akale abwinja; udzautsa maziko a mibadwo yambiri; udzatchedwa Wokonza pogumuka, Wakubwezera njira zakukhalamo.


Koma ndithu maziko a Mulungu aimika pokhazikika, ndi kukhala nacho chizindikiro ichi, Ambuye azindikira iwo amene ali ake; ndipo, Adzipatule kwa chosalungama yense wakutchula dzina la Ambuye.