Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 102:6 - Buku Lopatulika

Ndikunga vuwo m'chipululu; ndikhala ngati kadzidzi wa kumabwinja.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndikunga vuwo m'chipululu; ndikhala ngati kadzidzi wa kumabwinja.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Ndili ngati mbalame yakuchipululu, ngati kadzidzi wam'mabwinja.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ndili ngati kadzidzi wa ku chipululu, monga kadzidzi pakati pa mabwinja.

Onani mutuwo



Masalimo 102:6
8 Mawu Ofanana  

Fupa langa laumirira pa khungu langa ndi mnofu wanga, ndipo ndapulumuka ndili nazo nkhama za mano anga.


Ndinalankhulalankhula ngati namzeze, pena chumba; Ndinalira maliro ngati nkhunda; maso anga analephera pogadamira kumwamba. Ambuye ndasautsidwa, mundiperekere chikoli.


ndi nthiwatiwa, ndi chipudo, ndi kakowa, ndi kabawi mwa mtundu wake;


Chifukwa cha ichi ndidzachita maliro, ndi kuchema, ndidzayenda wolandidwa ndi wamaliseche; ndidzalira ngati nkhandwe, ndi kubuma ngati nthiwatiwa.


Ndipo zoweta zidzagona pansi pakati pake; nyama zonse za mitundumitundu; ndi vuwo ndi nungu zidzakhala m'mitu ya nsanamira zake; adzaimba mau ao m'mazenera; paziundo padzakhala chipasuko; pakuti anagadamula ntchito yake ya mkungudza.


Ndipo anafuula ndi mau olimba, nanena, Wagwa, wagwa, Babiloni waukulu, nusandulika mokhalamo ziwanda, ndi mosungiramo mizimu yonse yonyansa, ndi mosungiramo mbalame zonse zonyansa ndi zodanidwa.