Masalimo 102:5 - Buku Lopatulika5 Chifukwa cha liu la kubuula kwanga mnofu wanga umamatika kumafupa anga. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Chifukwa cha liu la kubuula kwanga mnofu wanga umamatika kumafupa anga. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Ndaonderatu ngati munthu wachitopa, ntchito yanga ndi kubuula nthaŵi zonse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Chifukwa cha kubuwula kwanga kofuwula ndatsala chikopa ndi mafupa okhaokha. Onani mutuwo |