Masalimo 102:4 - Buku Lopatulika4 Mtima wanga ukunga udzu womweta, nufota; popeza ndiiwala kudya mkate wanga. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Mtima wanga ukunga udzu womweta, nufota; popeza ndiiwala kudya mkate wanga. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Mtima wanga wakanthidwa, ndipo wafota ngati udzu, zoonadi, ngakhale chakudya chimandinyansa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Mtima wanga wakanthidwa ndipo ukufota ngati udzu; ndipo ndimayiwala kudya chakudya changa. Onani mutuwo |