Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Levitiko 11:16 - Buku Lopatulika

16 ndi nthiwatiwa, ndi chipudo, ndi kakowa, ndi kabawi mwa mtundu wake;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

16 ndi nthiwatiwa, ndi chipudo, ndi kakowa, ndi kabawi mwa mtundu wake;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

16 nthiŵatiŵa, chipudo, kakoŵa, akabaŵi a mitundu yonse,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

16 kadzidzi wamphondo, kadzidzi wodzuma, chipudo ndi mtundu uliwonse wa akabawi

Onani mutuwo Koperani




Levitiko 11:16
13 Mawu Ofanana  

Ndikunga vuwo m'chipululu; ndikhala ngati kadzidzi wa kumabwinja.


khwangwala mwa mtundu wake;


ndi nkhutukutu ndi nswankhono ndi manchichi;


Ndipo anafuula ndi mau olimba, nanena, Wagwa, wagwa, Babiloni waukulu, nusandulika mokhalamo ziwanda, ndi mosungiramo mizimu yonse yonyansa, ndi mosungiramo mbalame zonse zonyansa ndi zodanidwa.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa