Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Genesis 27:8 - Buku Lopatulika

Tsopanotu mwana wanga, tamvera mau anga monga momwe nditi ndikuuze iwe.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Tsopanotu mwana wanga, tamvera mau anga monga momwe nditi ndikuuze iwe.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Ndiye iwe mwana wanga, undimvere ndipo uchite zonse zimene ndikuuze.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Tsopano mwana wanga, mvetsetsa ndipo uchite zimene ndikuwuze:

Onani mutuwo



Genesis 27:8
8 Mawu Ofanana  

Yehova ndipo anati kwa iye, Mitundu iwiri ili m'mimba mwako, magulu awiri a anthu adzatuluka m'mimba mwako; gulu lina lidzapambana mphamvu ndi linzake; wamkulu adzakhala kapolo wa wamng'ono.


Ndipo amake anati kwa iye, Pa ine likhale temberero lako mwana wanga; koma tamvera mau anga, kazimuka kunditengera timeneto.


Ndipo tsopano mwana wanga, tamvera mau anga: tauka, nuthawire kwa Labani mlongo wanga ku Harani;


Unditengere ine nyama, undikonzere ine chakudya chokolera, kuti ndidzadye, ndi kudalitsa iwe pamaso pa Yehova, ndisanafe.


Pitatu kubusa, ukanditengere ine kumeneko tiana tiwiri tabwino tambuzi; ndikonzere nato chakudya chokolera cha atate wako chonga chomwe achikonda:


Koma Petro ndi Yohane anayankha nati kwa iwo, Weruzani, ngati nkwabwino pamaso pa Mulungu kumvera inu koposa Mulungu;


Ndipo anayankha Petro ndi atumwi, nati, Tiyenera kumvera Mulungu koposa anthu.


Ananu, mverani akukubalani mwa Ambuye, pakuti ichi nchabwino.