Genesis 25:23 - Buku Lopatulika23 Yehova ndipo anati kwa iye, Mitundu iwiri ili m'mimba mwako, magulu awiri a anthu adzatuluka m'mimba mwako; gulu lina lidzapambana mphamvu ndi linzake; wamkulu adzakhala kapolo wa wamng'ono. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201423 Yehova ndipo anati kwa iye, Mitundu iwiri ili m'mimba mwako, magulu awiri a anthu adzatuluka m'mimba mwako; gulu lina lidzapambana mphamvu ndi linzake; wamkulu adzakhala kapolo wa wamng'ono. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa23 Chauta adamuuza kuti, “M'mimba mwako muli mitundu iŵiri ya anthu. Udzabereka mafuko a anthu olimbana: mwana wina adzakhala wamphamvu kupambana mnzake, wamkulu adzakhala wotumikira wamng'ono.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero23 Yehova anati kwa iye, “Udzabala mafuko awiri a anthu olimbana, ndipo magulu awiri a anthu ochokera mwa iwe adzasiyana; fuko limodzi lidzakhala la mphamvu kuposa linzake, ndipo wamkulu adzatumikira wamngʼono.” Onani mutuwo |