Machitidwe a Atumwi 5:29 - Buku Lopatulika29 Ndipo anayankha Petro ndi atumwi, nati, Tiyenera kumvera Mulungu koposa anthu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201429 Ndipo anayankha Petro ndi atumwi, nati, Tiyenera kumvera Mulungu koposa anthu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa29 Koma Petro ndi atumwi enawo adati, “Tiyenera kumvera Mulungu koposa kumvera anthu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero29 Petro ndi atumwi enawo anayankha kuti, “Ife tiyenera kumvera Mulungu osati anthu! Onani mutuwo |