Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 27:7 - Buku Lopatulika

7 Unditengere ine nyama, undikonzere ine chakudya chokolera, kuti ndidzadye, ndi kudalitsa iwe pamaso pa Yehova, ndisanafe.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

7 Unditengere ine nyama, undikonzere ine chakudya chokolera, kuti ndidzadye, ndi kudalitsa iwe pamaso pa Yehova, ndisanafe.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

7 ‘Ubwere ndi nyama kuno, undiphikire. Nditadya, ndidzakudalitsa pamaso pa Chauta ndisanafe.’

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

7 ‘Bweretsere nyama yakutchire ndipo undikonzere chakudya chokoma kuti ndidye; kuti ndikudalitse pamaso pa Yehova ndisanamwalire.’

Onani mutuwo Koperani




Genesis 27:7
7 Mawu Ofanana  

Ndipo anamuka nakatenga nadza nato kwa amake; amake ndipo anakonza chakudya chokolera chonga chimene anachikonda atate wake.


nundikonzere ine chakudya chokolera chonga chomwe ndichikonda ine, nudze nacho kwa ine kuti ndidzadye; kuti moyo wanga ukadalitse iwe ndisanafe.


Ndipo Rebeka ananena kwa Yakobo mwana wake, nati, Taona ndinamva atate wako alimkunena ndi Esau mkulu wako kuti,


Tsopanotu mwana wanga, tamvera mau anga monga momwe nditi ndikuuze iwe.


Ndipo mdalitso, Mose munthu wa Mulungu anadalitsa nao ana a Israele asanafe, ndi uwu.


Ndipo Yoswa anawalumbirira nyengo ija, ndi kuti, Wotembereredwa pamaso pa Yehova munthu amene adzauka ndi kumanga mzinda uwu wa Yeriko; adzamanga maziko ake ndi kutayapo mwana wake woyamba, nadzaimika zitseko zake ndi kutayapo mwana wake wotsirizira.


Pakuti munthu akapeza mdani wake, adzamleka kodi kuti achoke bwino? Chifukwa chake Yehova akubwezere zabwino pa ichi unandichitira ine lero lomwe.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa