Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 27:6 - Buku Lopatulika

6 Ndipo Rebeka ananena kwa Yakobo mwana wake, nati, Taona ndinamva atate wako alimkunena ndi Esau mkulu wako kuti,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

6 Ndipo Rebeka ananena kwa Yakobo mwana wake, nati, Taona ndinamva atate wako alimkunena ndi Esau mkulu wako kuti,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

6 Rebeka adauza Yakobe kuti, “Ine ndamva bambo wako akuuza Esau kuti,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

6 Rebeka anati kwa mwana wake Yakobo, “Taona ndamva abambo ako akuwuza mʼbale wako Esau kuti,

Onani mutuwo Koperani




Genesis 27:6
3 Mawu Ofanana  

Ndipo Isaki anakonda Esau, chifukwa anadya nyama yake ya m'thengo; koma Rebeka anakonda Yakobo.


Ndipo anamva Rebeka pamene Isaki ananena ndi Esau mwana wake. Ndipo Esau ananka kuthengo kukasaka nyama ndi kubwera nayo.


Unditengere ine nyama, undikonzere ine chakudya chokolera, kuti ndidzadye, ndi kudalitsa iwe pamaso pa Yehova, ndisanafe.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa