Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 27:5 - Buku Lopatulika

5 Ndipo anamva Rebeka pamene Isaki ananena ndi Esau mwana wake. Ndipo Esau ananka kuthengo kukasaka nyama ndi kubwera nayo.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

5 Ndipo anamva Rebeka pamene Isaki ananena ndi Esau mwana wake. Ndipo Esau ananka kuthengo kukasaka nyama ndi kubwera nayo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

5 Rebeka ankangomvetsera pamene Isaki ankalankhula ndi mwana wake Esau. Tsono Esauyo atapita ku thengo kukasaka nyama yoti akapatse bambo wake,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

5 Koma Rebeka amamvetsera pamene Isake amayankhula ndi mwana wake Esau. Esau atanyamuka kupita kuthengo kukaphera abambo ake nyama,

Onani mutuwo Koperani




Genesis 27:5
2 Mawu Ofanana  

nundikonzere ine chakudya chokolera chonga chomwe ndichikonda ine, nudze nacho kwa ine kuti ndidzadye; kuti moyo wanga ukadalitse iwe ndisanafe.


Ndipo Rebeka ananena kwa Yakobo mwana wake, nati, Taona ndinamva atate wako alimkunena ndi Esau mkulu wako kuti,


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa