Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 27:8 - Buku Lopatulika

8 Tsopanotu mwana wanga, tamvera mau anga monga momwe nditi ndikuuze iwe.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

8 Tsopanotu mwana wanga, tamvera mau anga monga momwe nditi ndikuuze iwe.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

8 Ndiye iwe mwana wanga, undimvere ndipo uchite zonse zimene ndikuuze.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

8 Tsopano mwana wanga, mvetsetsa ndipo uchite zimene ndikuwuze:

Onani mutuwo Koperani




Genesis 27:8
8 Mawu Ofanana  

Yehova ndipo anati kwa iye, Mitundu iwiri ili m'mimba mwako, magulu awiri a anthu adzatuluka m'mimba mwako; gulu lina lidzapambana mphamvu ndi linzake; wamkulu adzakhala kapolo wa wamng'ono.


Ndipo amake anati kwa iye, Pa ine likhale temberero lako mwana wanga; koma tamvera mau anga, kazimuka kunditengera timeneto.


Ndipo tsopano mwana wanga, tamvera mau anga: tauka, nuthawire kwa Labani mlongo wanga ku Harani;


Unditengere ine nyama, undikonzere ine chakudya chokolera, kuti ndidzadye, ndi kudalitsa iwe pamaso pa Yehova, ndisanafe.


Pitatu kubusa, ukanditengere ine kumeneko tiana tiwiri tabwino tambuzi; ndikonzere nato chakudya chokolera cha atate wako chonga chomwe achikonda:


Koma Petro ndi Yohane anayankha nati kwa iwo, Weruzani, ngati nkwabwino pamaso pa Mulungu kumvera inu koposa Mulungu;


Ndipo anayankha Petro ndi atumwi, nati, Tiyenera kumvera Mulungu koposa anthu.


Ananu, mverani akukubalani mwa Ambuye, pakuti ichi nchabwino.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa