Genesis 27:8 - Buku Lopatulika8 Tsopanotu mwana wanga, tamvera mau anga monga momwe nditi ndikuuze iwe. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Tsopanotu mwana wanga, tamvera mau anga monga momwe nditi ndikuuze iwe. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Ndiye iwe mwana wanga, undimvere ndipo uchite zonse zimene ndikuuze. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Tsopano mwana wanga, mvetsetsa ndipo uchite zimene ndikuwuze: Onani mutuwo |