Genesis 27:9 - Buku Lopatulika9 Pitatu kubusa, ukanditengere ine kumeneko tiana tiwiri tabwino tambuzi; ndikonzere nato chakudya chokolera cha atate wako chonga chomwe achikonda: Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Pitatu kubusa, ukanditengere ine kumeneko tiana tiwiri tabwino tambuzi; ndikonzere nato chakudya chokolera cha atate wako chonga chomwe achikonda: Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Pita ku khola, ukanditengere timbuzi tiŵiri tonenepa bwino, kuti ndiphike, ndi kukonza chakudya chimene bambo wako amachikonda. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Pita ku khola, ukatenge ana ambuzi abwino awiri, kuti ndikonzere abambo ako chakudya chokoma monga amakondera. Onani mutuwo |