Genesis 27:10 - Buku Lopatulika10 ndipo udzapita nacho kwa atate wako, kuti adye, ndi kukudalitsa iwe asanafe. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 ndipo udzapita nacho kwa atate wako, kuti adye, ndi kukudalitsa iwe asanafe. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Ukapereke chakudyacho kwa bambo wako kuti akadye, ndipo akudalitse asanafe.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Kenaka upite nacho chakudyacho kwa abambo ako kuti adye ndi kukudalitsa asanafe.” Onani mutuwo |