Genesis 27:43 - Buku Lopatulika43 Ndipo tsopano mwana wanga, tamvera mau anga: tauka, nuthawire kwa Labani mlongo wanga ku Harani; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201443 Ndipo tsopano mwana wanga, tamvera mau anga: tauka, nuthawire kwa Labani mlongo wanga ku Harani; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa43 Tsopano mwana wanga, uchite zimene ndikuuze. Konzeka, thaŵira kwa mlongo wanga Labani ku Harani. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero43 Tsopano mwana wanga, chita zimene ndinene: Nyamuka tsopano, uthawire kwa mlongo wanga Labani ku Harani. Onani mutuwo |