Genesis 27:44 - Buku Lopatulika44 ukhale naye masiku akuwerengeka, mpaka utamchokera ukali mkulu wako; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201444 ukhale naye masiku akuwerengeka, mpaka wamchokera ukali wa mkulu wako; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa44 Bakakhala kwa iyeyo kanthaŵi ndithu, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero44 Ukakhale naye kwa kanthawi mpaka mkwiyo wa mʼbale wako utatsika. Onani mutuwo |