Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Genesis 26:13 - Buku Lopatulika

Ndipo analemera munthuyo, nalemera ndithu kufikira kuti anakhala wolemera kwambiri:

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo analemera munthuyo, nalemera ndithu kufikira kuti anakhala wolemera kwambiri:

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Chuma chake chidanka chichulukirachulukira, ndipo adasanduka munthu wolemera kwambiri.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Isake analemera. Chuma chake chinkachulukirachulukira mpaka anasanduka munthu wolemera kwambiri.

Onani mutuwo



Genesis 26:13
5 Mawu Ofanana  

Ndipo Abramu anali wolemera ndithu ndi ng'ombe ndi siliva ndi golide.


Yehova wamdalitsa mbuyanga kwambiri; ndipo analemera kwakulukulu; ndipo anampatsa iye nkhosa ndi ng'ombe, ndi siliva ndi golide, ndi akapolo ndi adzakazi, ndi ngamira ndi abulu.


Munthuyo ndipo analemera kwambiri, nali nazo zoweta zambiri, ndi akapolo aamuna ndi aakazi, ndi ngamira, ndi abulu.


M'nyumba mwake mudzakhala akatundu ndi chuma: Ndi chilungamo chake chikhala chikhalire.


Madalitso a Yehova alemeretsa, saonjezerapo chisoni.