Genesis 13:2 - Buku Lopatulika2 Ndipo Abramu anali wolemera ndithu ndi ng'ombe ndi siliva ndi golide. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Ndipo Abramu anali wolemera ndithu ndi ng'ombe ndi siliva ndi golide. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Abramu anali wolemera kwambiri. Anali ndi zoŵeta monga: nkhosa, mbuzi ndi ng'ombe, ndiponso siliva ndi golide yemwe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Abramu anali wolemera kwambiri; anali ndi ziweto ndiponso siliva ndi golide. Onani mutuwo |