Genesis 13:3 - Buku Lopatulika3 Ndipo anankabe ulendo wake kuchokera ku dziko la kumwera kunka ku Betele, kufikira kumalo kumene kunali hema wake poyamba paja pakati pa Betele ndi Ai; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Ndipo anankabe ulendo wake kuchokera ku dziko la kumwera kunka ku Betele, kufikira kumalo kumene kunali hema wake poyamba paja pakati pa Betele ndi Ai; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Kuchokera kumwera adasendera ndithu cha ku Betele, ku malo aja kumene kale adaamangako hema lake, pakati pa Betele ndi Ai. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Atachoka ku Negevi, anayenda malo osiyanasiyana mpaka anafika ku Beteli, ku malo a pakati pa Beteli ndi Ai, kuja kumene anamanga tenti poyamba, Onani mutuwo |