Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Genesis 13:3 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

3 Atachoka ku Negevi, anayenda malo osiyanasiyana mpaka anafika ku Beteli, ku malo a pakati pa Beteli ndi Ai, kuja kumene anamanga tenti poyamba,

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

3 Ndipo anankabe ulendo wake kuchokera ku dziko la kumwera kunka ku Betele, kufikira kumalo kumene kunali hema wake poyamba paja pakati pa Betele ndi Ai;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

3 Ndipo anankabe ulendo wake kuchokera ku dziko la kumwera kunka ku Betele, kufikira kumalo kumene kunali hema wake poyamba paja pakati pa Betele ndi Ai;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

3 Kuchokera kumwera adasendera ndithu cha ku Betele, ku malo aja kumene kale adaamangako hema lake, pakati pa Betele ndi Ai.

Onani mutuwo Koperani




Genesis 13:3
4 Mawu Ofanana  

Abramu anadutsa mʼdzikomo mpaka kukafika ku Sekemu pa mtengo wa thundu wa ku More. Nthawi imeneyo Akanaani analipobe mʼdzikomo.


Mose atawatuma kuti akazonde Kanaani anati, “Mupite kudzera ku Negevi, mukapitirire mpaka ku dziko la mapiri.


Ndi chikhulupiriro chomwecho anakhala ngati mlendo mʼdziko lija limene Mulungu anamulonjeza. Anakhala mʼmatenti monganso anachitira Isake ndi Yakobo, amene nawonso analonjezedwanso.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa