Genesis 30:43 - Buku Lopatulika43 Munthuyo ndipo analemera kwambiri, nali nazo zoweta zambiri, ndi akapolo aamuna ndi aakazi, ndi ngamira, ndi abulu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201443 Munthuyo ndipo analemera kwambiri, nali nazo zoweta zambiri, ndi akapolo aamuna ndi aakazi, ndi ngamira, ndi abulu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa43 Mwa njira imeneyi Yakobe adalemera kwambiri. Adakhala ndi zoŵeta zambiri, akapolo aamuna ndi aakazi, ngamira ndi abulu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero43 Mwa njira imeneyi, Yakobo analemera kwambiri ndipo anali ndi ziweto zochuluka kwambiri, antchito aakazi ndi aamuna, ngamira ndi abulu. Onani mutuwo |